Malawi yakumbukira asilikali omwe adamenya nawo nkhondo za dziko lapansi

Mwambo okumbukira asilikali omwe adamenya nkhondo ya dziko lonse lapansi udachitika lero ku chipilala chachikumbutso ku Cobbe Barracks ku Zomba. Wachiwiri kwa mtsogoleri wadziko lino a Saulos Chilima ndi yemwe adatsogolera mtundu wa a Malawi panwambowo. A Chilima adafika kumwambowo pomwe nthawi imangokwana 10:58 mamawa ndipo adayala nkhata yamaluwa pachipilala chachikumbutsochocho. Kuno ku Malawi mwambowu […]

The post Malawi yakumbukira asilikali omwe adamenya nawo nkhondo za dziko lapansi appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください