Makosana a MRA abilibinya Jetu – Dorothy Kingston

Dorothy Kingston wadandaula zakhalidwe lomwe achita akuluakulu a Malawi Revenue Authority (MRA) komaso apolisi munzinda wa Lilongwe omwe akuti awazunza komaso kumumenya woyimba wachikulire Jetu. Dorothy yemwe ndi nkazi wake wa woyimba Zeze Kingston, wati gogo wa zaka 72-yu pamodzi ndi iye akumana ndi tsokali Lachinayi madzulo pomwe amabwelera ku Blantyre kuchokera ku Lilongwe komwe […]

The post Makosana a MRA abilibinya Jetu – Dorothy Kingston appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください