Maesiteti ku Thyolo azipereka msonkho ku khonsolo

Khonsolo ya boma la Thyolo yapanga lamulo loti eni minda ikuluikulu ya tiyi adzipereka msonkho ku khonsoloyi. Wapampando wa khonsoloyi, Rhustin Banda, ndiye watsimikiza za nkhaniyi. A Banda ati kwa nthawi yaitali eni mindayi samalipira msonkho wa pa chaka ku khonsoloyi ngakhale amapanga phindu lochuluka chifukwa chosowa lamulo. “Minsonkhoyi ithandizira kupititsa pa tsogolo zitukuko za […]

The post Maesiteti ku Thyolo azipereka msonkho ku khonsolo appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください