Mabungwe ati apolisi kwa Jenda agwire ntchito mosaona nkhope

Wapampando wa mabungwe omwe asali aboma ku Mzimba a Christopher Melele ati  ndiwokhuzidwa kwambiri kuti adindo ena  akulephera ntchito m’bomali. Iwo adzudzula zomwe zikuchitika kuti apolisi ya Jenda akukanika kukwizinga mwana wa Inkhosi Khosolo  wazaka 25 zakubadwa komanso yemwe ndiwogwira ntchito m’boma, pomwe maumboni woti munthuyo anakwatira msikana wachichepera wazaka 15,ulipo. Melele wati sakuwona chifukwa […]

The post Mabungwe ati apolisi kwa Jenda agwire ntchito mosaona nkhope appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください