Ma Membala a PAC apewe kulandira ma udindo kuchokera kwa mtsogoleri wa dziko

Woyankhulira chipembedzo cha chisilamu Sheikh Dinala Chabulika wati dziko lino likumagawanika chifukwa cha mipingo maka ikaonetsa chidwi pa amene anthu akhonza kudzamsankha pa masankho a mtsogoleri wa dziko ndipo ati nthawi yakwana tsopano kuti atsogoleri a bungwe la Public affairs Committee (PAC) asamalandile ma udindo kuchokera kwa mtsogoleri wa dziko. Poyankhula lero mu pologamu ya […]

The post Ma Membala a PAC apewe kulandira ma udindo kuchokera kwa mtsogoleri wa dziko appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください