Loya wanjatidwa kamba kogula galimoto yobedwa ku South Africa

Katswiri pa nkhani za malamulo a Stanley Chirwa omwe amayimilira anthu pa milandu, ali m’manja mwa apolisi powaganizira kuti anagula galimoto yomwe inabedwa m’dziko la South Africa ndi zigawenga zokhala ndi mfuti. Ofalitsa nkhani za a Polisi m’dziko muno, a Peter Kalaya, ndi omwe atsimikiza za nkhaniyi ponena kuti a Chirwa amangidwa kumapeto kwa sabata […]

The post Loya wanjatidwa kamba kogula galimoto yobedwa ku South Africa appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください