Livingstonia Synod ipempha boma kuti lichose msonkho wapamalipiro a azibusa awo

Bungwe la Church and Society mu mpingo wa CCAP mu Synod ya Livingstonia, lapempha boma, ku bungwe lotolera misonkho la MRA, kuti lichotse msonkho wapa malipiro a azibusa a mpingowu. Iwo ati ndi abusa a mpingo okhawu mu CCAP omwe amalipira msonkho wa PAYE pomwe anzizawo mu ma synod a Blantyre ndi Nkhoma satelo ayi. […]

The post Livingstonia Synod ipempha boma kuti lichose msonkho wapamalipiro a azibusa awo appeared first on Malawi Nyasa Times – News from Malawi about Malawi.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください