Zomwe yachita nduna yakale ya boma la m’gwirizano wa Tonse a Timothy Mtambo podzudzula boma pa mavuto omwe akuta dziko lino zadzidzimutsa akatswiri komanso anthu m’dziko lino. Pothilira ndemanga pa zomwe a Mtambo anena dzulo pa msonkhano wa atolankhani mu mzinda wa Lilongwe pomwe anati utsogoleri wa pulezident Chakwera walephera kuthetsa mavuto omwe a Malawi […]
The post Lero limenelo? – Amalawi afunsa Mtambo appeared first on Malawi 24.