Kuno ayi ti anthu ta katangale inu – dziko la USA lauza a Matemba ndi ena kuti asazapitenso ku Amereka

Ngati sanapiteko ndi komwe ndiye nyimbo ya Buffalo Soldier ya a Gidess Chalamanda asiya kumvera. Koma ngati anapondako kale ati asazabwelerekonso. Dziko la United States of America lalengeza kuti ena mwa adindo a dziko lino asadzapitekonso ati kamba ali ndi chifungo cha katangale. Izi zili mu kalata imene dzikoli latulutsa lero. Malinga ndi kalatayi, amene […]

The post Kuno ayi ti anthu ta katangale inu – dziko la USA lauza a Matemba ndi ena kuti asazapitenso ku Amereka appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください