Kuno ayi – ansembe Akatolika aletsedwa kudalitsa maukwati a amuna kapena akazi okhaokha

Ma bishopu a mpingo wa Katolika pansi pa bungwe lawo la Episcopal Conference of Malawi (ECM), ati zomwe wanena mtsogoleri wa mpingowu papa Francis sizikutanthauza kuti mpingowu waloleza maukwati a amuna kapena akazi okhaokha ndipo anenetsa kuti palibe wansembe amene aloledwe kudalitsa maukwati oterewa kuno ku Malawi. Izi zikudza kutsatira nkhani yomwe yadziwika lachiwiri pa […]

The post Kuno ayi – ansembe Akatolika aletsedwa kudalitsa maukwati a amuna kapena akazi okhaokha appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください