Ku Malawi kwabadwa chipani china Cha PDP

Mtsongoleri wazipani zotsutsa boma kunyumba yamalamulo yemwenso ndi phungu wanyumba yamalamulo wa dera lapakati m’boma la Mulanje Kondwani Nankhumwa walengeza kuti wayambitsa chipani chake cha People’s Development Party (PDP). A Nankhumwa, womwe anachotsedwa mu chipani cha Democratic Progressive Party (DPP) alengeza izi patsamba lawo la mchenzo la Facebook. Nankhumwa wanena kuti apangitsa msonkhano wa atolankhani […]

The post Ku Malawi kwabadwa chipani china Cha PDP appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください