Boma lauza khonsolo ya mzinda wa Lilongwe (LCC) kuti lisiye kutchetcha chimanga chomwe chinalimidwa mu madera ena a mzinda wa Lilongwe. Khonsolo ya Lilongwe dzulo yakhala ikutchetcha chimanga mu m’madera a Area 43 ndi 11 ponena kuti malamulo salola anthu kulima pa mapuloti kapena m’mbali mwa nsewu mu mzindawu. M’modzi mwa akuluakulu oyang’anira zinthu zosiyanasiyana […]
The post Khonsolo ya Lilongwe ailetsa kutchetcha chimanga appeared first on Malawi 24.
Moni Malawi 
