Khanda lapsera m’nyumba mai ake atapita kokathyoletsa khobwe

Khanda la miyezi isanu ndi iwiri, lafa pomwe nyumba yomwe linagonekedwamo usiku lokhalokha inayaka moto pa nthawi yomwe mai ake anapita kokachita zadama ku nyumba kwa njonda ina. Watsimikiza za nkhaniyi ndi wofalitsa nkhani pa polisi ya boma la Kasungu a Joseph Kachikho omwe azindikira khandali ngati Ethel Petuli pomwe mai ake azindikilidwa ngati Mtisunge. […]

The post Khanda lapsera m’nyumba mai ake atapita kokathyoletsa khobwe appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください