Katswiri pa ulimi wati zoti dziko lino likolora chakudya chochuluka zikupereka mafunso

M’modzi mwa akatswiri pa nkhani za ulimi a Leonard Chimwanza, wati zotsatira zomwe unduna wa za ulimi watulutsa ponena kuti dziko lino likolola chakudya chochuluka ndizodzetsa mafunso kutengera ndi momwe mbewu ziliri m’minda yambiri mdziko muno. Malingana ndi a Chimwanza, pakadali pano aliyense akutha kudzionera yekha momwe mbewu zaumira m’minda yochuluka kaamba kavuto lang’amba. Iwo […]

The post Katswiri pa ulimi wati zoti dziko lino likolora chakudya chochuluka zikupereka mafunso appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください