Katswiri pa nkhani za ndale wati boma lachita chamuna pothetsa milandu ya anthu osokoneza m’dipiti

M’modzi mwa akatswiri omwe amayankhulapo pa nkhani za mdziko muno, a Lyford Chadza, ayamikira boma kaamba kothetsa mlandu wa anthu atatu omwe adanjatidwa kamba kosokoneza galimoto zapa m’dipiti ponena kuti izi zidakaononga ubale wabwino pakati paboma ndi anthu aku Ndirande. Malingana ndi a Chadza, ati zomwe lachita boma ndichiyambi chokonza ndikumanga ubale wabwino pakati pa […]

The post Katswiri pa nkhani za ndale wati boma lachita chamuna pothetsa milandu ya anthu osokoneza m’dipiti appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください