Kalindo akuchititsa zionetsero ku Zomba

Mtsogoleri wa Malawi First Bon Kalindo ali mu mzinda wa Zomba kuchita ziwonetsero zosakondwa ndi kugwa kwa mphamvu ya kwacha, kukwera kwa mitengo ya zinthu komanso kuchepa kwa malipiro anthu ogwira ntchito Boma. Ziwonetserozi zayambira pa bwalo laza masewero la Zomba Community Ground mpaka akapereke chikalata chamadandaulo ku office ya Bwana Mkubwa wa Boma la […]

The post Kalindo akuchititsa zionetsero ku Zomba appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください