Ine ndiye Mose ine – watero Timothy Mtambo

Mudziwitseni Phungu Joseph Nkasa kuti analakwitsa. Mose wa lero ati sanali Mutharika, koma ndi a Timothy Mtambo. Atero eniake pomwe anapangitsa msonkhano wa atolankhani lero pofuna kukumbutsa kuti akadalipo. A Mtambo amene adachita chete pomwe boma la Tonse lidawapatsa unduna, ndipo samamvekabe ngakhale atachotsedwa, pa 27 April achititsa msonkhano wa atolankhani ku Lilongwe. Msonkhanowu omwe […]

The post Ine ndiye Mose ine – watero Timothy Mtambo appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください