Genda galu kuti udziwe mwini wake: kuchotsedwa kwa anthu ku DPP kwakwiyitsa MCP

Chipani cha Malawi Congress (MCP) chati ndichokhumudwa ndi zomwe chapanga chipani cha Democratic Progressive (DPP) pochotsa ma membala ake ena mu chipanicho kuphatikiza a Kondwani Nankhumwa; koma anthu ena akuti ukafuna kudziwa mbuyake wa galu, umatola duka ndikum’gweba nalo pomwe ena akuti agalu otumidwa aja adya zothira tameki ndipo mwini agaluwo wakwiya. Nkhaniyi yayamba pomwe […]

The post Genda galu kuti udziwe mwini wake: kuchotsedwa kwa anthu ku DPP kwakwiyitsa MCP appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください