Flames ithambitsana ndi Chipolopolo lero pa Bingu Stadium

Timu ya mpira wa miyendo ya dziko lino Flames lero pa 26 March ikuyembekezereka kuthambitsana ndi Chipolopolo ya m’dziko la Zambia kulimbirana malo achitatu mu 4 Nations Tournament ndipo masewero ake ayamba 2 koloko masana. Lero lomwe lino, Zimbabwe ikomana ndi Kenya kulimbirana malo woyamba ndipo masewero ake ayamba 5 koloko madzulo. Zimbabwe inafika mu […]

The post Flames ithambitsana ndi Chipolopolo lero pa Bingu Stadium appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください