DPP ikudzudzulidwa polephera kusamala maliro a membala wake

Anthu m’masamba anchezo akulavulira zakukhosi chipani chotsutsa cha DPP pa malipoti oti chinakana kuthandiza membala wake yemwe wamwalira atadwala ku mwambo oyika m’manda malemu Goodall Gondwe. Malipoti akuti DPP inakananso kunyamula thupi lake, ati poti analibe udindo ku chipani. Tsamba lino lamvetsedwa kuti m’modzi mwa akafa ndikhale a chipani cha DPP, Criff Ngomango, anadandaula kuti […]

The post DPP ikudzudzulidwa polephera kusamala maliro a membala wake appeared first on Malawi24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください