DoDMA yati mabanja a ulesi sazilandira chimanga chaulere kuchokela ku Boma

Nthambi yoona za ngozi zogwa mwadzidzi m’dziko muno ya Department of Disasters Management Affairs (DoDMA) yati mabanja omwe   ali ndikuthekera kogwira ntchito koma ndi a ulesi sazilandira thandizo la chimanga kuchokera ku Boma. Wanena izi ndi Mlembi Wamkulu ku nthambiyi, Charles Kalemba, m’mudzi mwa mfumu yaikulu Tengani m’boma la Nsanje, pomwe adapita kukakambirana ndi adindo […]

The post DoDMA yati mabanja a ulesi sazilandira chimanga chaulere kuchokela ku Boma appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください