Pamene anthu akupitilira kukakamiza nduna yowona za mphamvu ya magetsi a Ibrahim Matola kuti apepese pazomwe anayankhula dzulo m’boma la Dedza, a Matola ati anthu sakutanthauzira bwino mwambi omwe iwo anapeleka. A Matola akudzudzulidwa kaamba konena kuti anthu omwe akudandaula kuti a Lazarus Chakwera akuyendayenda kwambiri ndi achule. Potsatira nkhaniyi, anthu oyankhula pazinthu zosiyanasiyana komaso […]
The post Chule anakana m’madzi muli mwake: a Matola ati a Malawi atanthauzira molakwika mwambi wawo appeared first on Malawi 24.