Choipa chitsata mwini: sitima yanyenya mwendo wa ofuna kuba mafuta

Mnyamata wina wa zaka 18 ku Balaka ali mu ululu owopsa pomwe wanyenyedwa mwendo ndi sitima yomwe anaidumphira ikuyenda kuti akabemo mafuta. Malingana ndi ofalitsa nkhani pa polisi ya Balaka a Gladson M’bumpha, ovulazidwayu wazindikilidwa ngati a Lawrence Yakobe omwe akumana ndi zakudazi lachitatu pa 22 November, 2023. A M’bumpha ati Yakobe anadumphira sitima ya […]

The post Choipa chitsata mwini: sitima yanyenya mwendo wa ofuna kuba mafuta appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください