Chizungu chikucheka ma galajuweti amene – atero a UNIMA

Zadziwika kuti ophunzira ambiri a mu sukulu za ukachenjede chingerezi chikumawapeta ndipo ambiri sakwanitsa kufotokoza komanso kulemba m’chizungu chomveka bwino. Izi ndi malingana ndi otsatira kwa wachiwiri wa Chancellor ku sukulu ya ukachenjede ya University of Malawi (UNIMA), Dr Sunduzwayo Madise yemwe wati kusowa kwa ukadaulo pa kaphunzitsidwe kamakono maka kuyambira ku m’mela mpoyamba kukuwonjezera  kuvutika […]

The post Chizungu chikucheka ma galajuweti amene – atero a UNIMA appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください