Chipani cha DPP chati Mutharika ndiye yankho la a Malawi

Chipani cha Democratic Progressive Party (DPP) chati Peter Mutharika ndiye yankho la a Malawi ndipo ngati mtsogoleri wachipanichi ndiwokonzeka kudzapikisana nawo pachisankho cha 2025. Gavanala wachipani cha DPP mchigawo chakum’mawa a Imran Ntenje ndi womwe ayankhula izi pomwe chipanichi chidakonza misonkhano yoyimaima yomwe akuyitchula kuti Blue Convoy mu boma la Zomba. A Ntenje adati malo […]

The post Chipani cha DPP chati Mutharika ndiye yankho la a Malawi appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください