Chikhulupiliro cha anthu chili mwa UTM – atelo a Kaliati

Pomwe masiku akusendera ku chitseko kuti dziko lino lichititse chisankho chaka cha mawa, mlembi wa chipani cha UTM a Patricia Kaliati ati ndiothokoza kuti chikhulupiliro cha anthu ochuluka mdziko muno chili mwa chipani chawo koma ati afotokozabe posachedwapa ngati chipanichi chipitilire kukhalabe mu mgwirizano wa Tonse kapena ayi. A Kaliati ayankhula izi pomwe amacheza ndi […]

The post Chikhulupiliro cha anthu chili mwa UTM – atelo a Kaliati appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください