Chakwera wakhululukira Mussa John

Mtsogoleri wa dziko lino Lazarus Chakwera wakhululukira Mussa John yemwe chaka chatha analamulidwa kukakhala ku ndende kwa zaka zitatu atapezeka olakwa pa mlandu opezeka ndi chamba. Nduna ya za mdziko a Zikhale Ng’oma atsimikiza kuti John ndi m’modzi wa akaidi 200 omwe akhululukidwa potengera nyengo ino yokumbukira kufa ndi kuuka kwa Ambuye Yesu. John anapezeka […]

The post Chakwera wakhululukira Mussa John appeared first on Malawi24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください