Chakwera ayankhanso Mutharika: ulamuliro wanga wakumana ndi zokhoma zambiri ndi chifukwa ndalephera

Iyi ithera ku waya ndithu. Mtsogoleri wa dziko lino a Lazarus Chakwera akuoneka kuti sanathane ndi moto omwe owatsutsa a Peter Mutharika adayatsa ku Blantyre lamulungu lapitali pa msonkhano wawo wandale. Adakapitiriza kuwayankha mokuluwika. Lero lachinayi a Chakwera adzudzula atsogoleri omwe akupitiriza kuwanena kuti ndiolephera. Iwo anena izi mu mzinda wa Lilongwe. A Chakwera ati […]

The post Chakwera ayankhanso Mutharika: ulamuliro wanga wakumana ndi zokhoma zambiri ndi chifukwa ndalephera appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください