Chakwera ayamikila Bungwe la Red Cross kamba ka ntchito zabwino zomwe bungweli lakhala likupanga

Mtsogoleri wadziko lino Dr Lazarus Chakwera lero wakumana ndi mlembi wamkulu wa bungwe la International Federation of Red Cross (IFRC) kuno ku Malawi a Jagannath Chapagain yemwe wangosankhidwa kumene. Mmawu ake a Chakwera ayamikira bungwe la International Federation of Red Cross chifukwa cha thandizo lomwe bungweli limapereka kudziko la Malawi. A Chakwera anathokoza bungweli maka […]

The post Chakwera ayamikila Bungwe la Red Cross kamba ka ntchito zabwino zomwe bungweli lakhala likupanga appeared first on Malawi Nyasa Times – News from Malawi about Malawi.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください