Chakwera apempha apolisi kuti akhale osunga mwambo

Mtsogoleri wadziko lino a LazarusChakwera yemwenso ndi wamkulu kunthambi ya a polisi, wapempha apolisi mdziko muno kuti akhale anthu osunga mwambo. Mukulankhula kwawo ku mwambo otsanzikana ndi ophunzira ku sukulu zanthambiyi, ku Blantyre, a Chakwera adati zimakhala zomvetsa chisoni kuona a Polisi kukhalanso oyamba kumphwanya malamulo. A Chakwera adati a Polisi ndi anthu ofunika kwambiri […]

The post Chakwera apempha apolisi kuti akhale osunga mwambo appeared first on Malawi Nyasa Times – News from Malawi about Malawi.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください