Chakwera apempha Amalawi kuti achilimike pa ntchito yotukula dziko

Mtsogoleri wa dziko lino Dr Lazarus McCarthy Chakwera wapempha Amalawi kuti achilimike pa ntchito yotukula madera awo posadalira kuti ena adzawagwirire ntchitoyo. Chakwera anena mauwa m’boma la Nkhata Bay Lamulungu pamwambo wokumbukira omwe adaphedwa ndi azungu pomenyera ufulu wa dziko lino. Iwo adati Amalawi ayenera kuphunzira kwa ‘makolo athu’ omwe adagwiritsa ntchito zipangizo zomwe zidalipo […]

The post Chakwera apempha Amalawi kuti achilimike pa ntchito yotukula dziko appeared first on Malawi Nyasa Times – News from Malawi about Malawi.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください