Chakwera alamulira 2030 woo, atero a Chimwendo-Banda

Nduna yowona za maboma ang’ono a Richard Chimwendo Banda ati amene akulota kuti alowanso m’boma apitilize kulota kamba koti m’tsogoleri wa dziko lino a Lazarus Chakwera alamulira mpaka 2030. Ndunayi yayankhula izi pa chikondwelero chokumbukira mtsogoleri oyamba wadziko lino Malemu Ngwazi Dr. Hastings Kamuzu Banda ku Blantyre pa Kamuzu Stadium. A Chimwendo anati Kamuzu anali […]

The post Chakwera alamulira 2030 woo, atero a Chimwendo-Banda appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください