Bushiri wayamba kugawa chimanga cha ndalama zokwana 14 biliyoni

Prophet Shepherd Bushiri yemwe ndi mtsogoleri wa mpingo wa Enlightened Christian Gathering (ECG) walengeza kuti wayamba pologalamu yogawa chimanga kwa maanja oposa 1 miliyoni omwe akhudzidwa ndi njala mdziko muno. Malingana ndi a Bushiri omwe amayankhula izi kunkhokwe yosungira chimangachi, chimangachi chilipo chokwana 17,000 Metric tons, ndipo ndichandalama zokwana 14 biliyoni Malawi kwacha. Bushiri wapemphanso […]

The post Bushiri wayamba kugawa chimanga cha ndalama zokwana 14 biliyoni appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください