Bushiri wagawa chimanga kwa anthu 18,000 ku Lilongwe

Pomwe akupitilira ndi ntchito yogawira chimanga anthu omwe akhudzidwa ndi njala m’dziko muno, mtsogoleri wa mpingo wa Enlightened Christian Gathering (ECG), Mneneri Shepherd Bushiri, wagawa chimanga kwa anthu opitilira 18,000 munzinda wa Lilongwe. Mneneri Bushiri wagawa chimangachi Lamulungu pa 17 March, 2024 kulikulu la ofesi yake ku Golden Peacock mu mzinda wa Lilongwe komwe khwimbi […]

The post Bushiri wagawa chimanga kwa anthu 18,000 ku Lilongwe appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください