Bushiri wagawa Chimanga ku Nkhotakota

Prophet Shepherd Bushiri yemwe ndi mtsogoleri wa mpingo wa ECG – The Jesus Nation, lero wagawa chimanga kwa anthu opitilira 1300 mdera la Sub-T/A Nkhanga m’boma la Nkhotakota. Polankhula pa mwambo ogawa chimangacho kudzera kwa mneneri wawo, a Aubrey Kusakala, prophet Bushiri wati ndiokhudzidwa kwambiri ndi kutaika kwa miyoyo komaso kuonongeka kwa katundu kamba ka […]

The post Bushiri wagawa Chimanga ku Nkhotakota appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください