Bushiri athandiza mwana odyetsedwa dowe wamuwisi

Mtsogoleri wa mpingo wa Enlightened Christian Gathering (ECG) Shepherd Bushiri wati ayamba kuthandiza mwana yemwe posachedwapa anaonesedwa m’masamba a nchezo akudyetsedwa dowe wa muwisi. Posachedwapa, anthu ambiri m’masamba a nchezo anagwidwa ndi chisoni kamba ka kanema yemwe anthu anamugawana kwambiri yemwe amaonetsa mwana wina wa zaka khumi ndi ziwiri (12) akudyetsedwa mondokwa wa muwisi. Malipoti […]

The post Bushiri athandiza mwana odyetsedwa dowe wamuwisi appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください