Bon Kalindo wamangidwanso bwalo ku Zomba litamupatsa belo

Bwalo la Principal Resident Magistrate ku Zomba lapereka belo kwa mkulu wa Bungwe la Malawi First a Bon Kalindo koma apolisi amanganso a Kalindo atangotuluka mu bwalo la milandu pankhani yokhudza zipolowe za ku Mangochi pa nthawi yomwe adachititsa mademo. Bwaloli linakana pempho lomwe adapempha woyimira Boma pamilandu loti a Kalindo asawapatse belo kuwopa kuti […]

The post Bon Kalindo wamangidwanso bwalo ku Zomba litamupatsa belo appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください