Boma silikugwirizana ndi chipepeso cha K103 miliyoni kwa Brian Banda

Boma kudzera kwa mlangizi wake pa za malamulo lati likukonza zoti likasume kutsutsana ndi chigamulo choti lipeleke ndalama yokwana K103 miliyoni kwa a Brian Banda ngati chipepeso powachotsa ntchito ya mneneri wa mtsogoleri wa dziko lino a Lazarus Chakwera. M’mwezi wa August mchaka cha 2020, a Banda omwe pano akugwira ntchito ngati mtolankhani ku Times […]

The post Boma silikugwirizana ndi chipepeso cha K103 miliyoni kwa Brian Banda appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください