Boma likuyembekezeka kugawa masikito mdziko muno

Boma lati ligawa masikito otetezera ku udzudzu mzigawo zonse m’dziko muno pofuna kuthana ndi nthenda ya malungo yomwe ikadaperekabe chiwopsezo chachikulu pa umoyo ndipo ntchitoyi igwilika ndi thandizo la ndalama pafupifupi 84 biliyoni kwacha lomwe ipeleke ndi bungwe la Global fund. Malingana ndi m’modzi mwa akuluakulu ku nthambi ya unduna wa za umoyo mdziko muno, […]

The post Boma likuyembekezeka kugawa masikito mdziko muno appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください