Boma likufuna limange bwalo la masewero kwa Nsundwe

Pomwe bwalo ya Kamuzu ili chikalambire ku Blantyre, dera lomwe linatchuka kwambiri nthawi ya ziwonetsero m’chaka cha 2019, Nsundwe, lalandira mphoto ya bwalo lochitilapo masewero lomwe boma lalengeza kuti likufuna kumanga kudelali. Nkhaniyi yadziwika pomwe khonsolo ya mzinda wa Lilongwe yatulutsa chikalata chomemeza ma kampani omanga kuti yomwe ingachite mphumi igwire ntchito. Chikalatachi chikusonyeza kuti […]

The post Boma likufuna limange bwalo la masewero kwa Nsundwe appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください