Boma ligayitsa chimanga chomwe linalanda chochokera ku Tanzania

Ngati njira imodzi yofuna kupewera matenda a chimanga omwe agwa mdziko la Tanzania kuyambukira mdziko muno, boma la Malawi lati likagayitsa chimanga chomwe linalanda anthu ena omwe amafuna achilowetse mdziko muno. Izi zikudza pomwe boma la Malawi kumapeto a chaka chatha linaletsa aliyese kulowetsa m’dziko muno chimanga chochokera mdziko la Tanzania komanso Kenya ati pofuna […]

The post Boma ligayitsa chimanga chomwe linalanda chochokera ku Tanzania appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください