Boma latsindika kuti limanga mabwalo amasewera a Bullets ndi Wanderers

Boma latsindika ku mtundu wa a Malawi kuti limanga mabwalo amasewero a matimu a Mighty Mukuru Wanderers komanso FCB Nyasa Big Bullets mu mzinda wa Blantyre. Nduna yoona za achinyamata ndi masewero mdziko muno a Uchizi Mkandawire ndi omwe atsindika za nkhaniyi. Ntchito yomanga mabwalo amasewerawa alengezedwa koyamba mchaka cha 2020 koma idayamba yayima kaye. […]

The post Boma latsindika kuti limanga mabwalo amasewera a Bullets ndi Wanderers appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください