Boma lati likubweza ngongole ya US$800 miliyoni yomwe inatenga DPP

Boma la mgwirizano wa Tonse lati likubweza ngongole ya US$800 miliyoni yomwe linatenga boma la chipani cha DPP ndipo izi zikuchititsa kuti ndalama zakunja zizisowa m’dziko muno. Wanena izi ndi nduna yofalitsa nkhani a Moses Kunkuyu omwe amayankhula lero pa msonkhano wa olemba nkhani ku Lilongwe. Msonkhanowu unapangidwa kuti boma lifotokoze bwino chifukwa chimene mafuta […]

The post Boma lati likubweza ngongole ya US$800 miliyoni yomwe inatenga DPP appeared first on Malawi24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください