Boma la Mwanza lakwanitsa kuthesa ma ukwati a ana okwana 118

Mkulu wa Mwanza Social Welfare, a Mary Msidwa, ati boma la Mwanza lakwanitsa kuthetsa maukwati a ana achichepere okwana 118 mu chaka cha 2023. A Msindwa anena izizi lero pamene anali ndi zokambilana  ndi khosolo la boma la Zomba komaso bungwe la Save the Children pa mutu oti “Kuthetsa maukwati a ana achichepere”. Iwo ati […]

The post Boma la Mwanza lakwanitsa kuthesa ma ukwati a ana okwana 118 appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください