Boma alipempha kuti lichite changu popeleka zipangizo za ulimi

Phungu wa nyumba ya malamulo wa dera lapakati mu mzinda wa Lilongwe Alfred Jiya wapempha boma kuti lichite machawi popeleka zipangizo za ulimi zotsika mitengo kwa anthu okhala m’madera amatawuni ponena kuti nawo ali ndi minda komanso amafuna kukhala ndi chakudya chokwanila. Iye walakhula izi m’nyumba ya malamulo lachiwiri sabata ino pomwe anafunsa funso nduna […]

The post Boma alipempha kuti lichite changu popeleka zipangizo za ulimi appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください