Bambo wazaka 44 ali mchitokosi chifukwa chogwirilira anyamata

Bambo wa zaka 44 amumanga ku Mchinji chifukwa chogwirilira anyamata awiri a zaka zosaposera 12. Wofalitsa nkhani za apolisi ku Mchinji a Limbani Mpinganjira wati bamboyu dzina lake ndi James Makunganya. Malingana ndi a Mpinganjira, bamboyu aampereka K500 kwa anyamatawa komanso amawaopseza kuti awapha akakawulula kwa makolo awo. Koma anawa tsiku lina analimba mtima ndikuwawuza […]

The post Bambo wazaka 44 ali mchitokosi chifukwa chogwirilira anyamata appeared first on Malawi24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください