Bambo wapha mkazi wake pomumenya m’mutu ndi mwala

Bambo wa zaka 32 yemwe dzina lake ndi  Dickson Kachikuni ali mu chitokosi cha a polisi ya pa Nkhunga ku Nkhotakota kamba kowaganizira kuti apha mkazi wawo Leah Ngoma wa zaka 21 pomumenya ndi mwala m’mutu  pomwe amagona usiku wapa 1 January. Bamboyu akuti amaganizira kuti mkazi wakeyu anali ndi chibwenzi chamseli. Mneneli wapolisi ya […]

The post Bambo wapha mkazi wake pomumenya m’mutu ndi mwala appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください