Bambo wadzipha ataba nkhuku

Bambo wa zaka 38 mu mzinda wa Lilongwe wadzipha podzimangilira  ku denga la nyumba yake atazindikira kuti abale ake adziwa kuti iye anaba nkhuku ya m’bale wake. Watsimikiza za nkhaniyi ndi wachiwiri kwa ofalitsa nkhani pa polisi ya munzinda wa Lilongwe mayi Khumbo Sanyiwa omwe azindikira malemuwa ngati a Davison Sitima. Sanyiwa wati bambo Sitima […]

The post Bambo wadzipha ataba nkhuku appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください