Bambo wa zaka 24 wamangidwa chifukwa chokupha mwana wa mlongo wake

A Phillip Mwanza a zaka 24 awamanga kwa Jenda ku Mzimba powaganizira kuti apha mwana wa mlongo wawo, a Steven Shaba, a zaka 21, ndewu itabuka kamba ka suti yovala pa ukwati Mneneri wa Polisi ya Jenda a Macfarlane Mseteka ati izi zachitika dzulo ku Vibangalala m’bomali. A Mseteka ati a Mwanza anapsa mtima kamba […]

The post Bambo wa zaka 24 wamangidwa chifukwa chokupha mwana wa mlongo wake appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください