Azipita Chamkakala – a mabungwe

Atha kuona ma demo angati a Jane Ansah naye Masautso Chamkakala chifukwa a mabungwe ndiye akwiya naye. Ati sakuona phindu lake.  Mabungwe omwe si aboma ati a Chamkala omwe ndi mkulu wa ofesi ya yoyang’anira zozenga milandu m’dziko muno, Director of Prosecutions (DPP), akuyenera kutula pansi udindo polephera kugwira ntchito yake moyenera.  Izi zanenedwa pa […]

The post Azipita Chamkakala – a mabungwe appeared first on Malawi 24.

マラウイニュースメルマガ登録

メルマガ限定配信のマラウイ超ローカルニュースが無料で受け取れます

マラウイ・アフリカ・国際協力に興味があったら登録しよう!

プライバシーポリシーについてはこちらを確認してください